Lyrics Gwamba – Akondakitale

Akondakitale Lyrics – Gwamba

Singer: Gwamba
Title: Akondakitale

Yi, aye-iye-yah
Aye-iye-yah
Akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
Akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje

Ulendo wanga ukathera ku Lilongwe, m’deport
Koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje
Inu ulendo wanga ukathera ku Lilongwe, m’deport
Koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje, yi

Aish, ndalama nde yavuta pa nyasa
Daily fans kumayisaka
Sikuwona zoti ndiwe shasha
Kumenya business basi kumayitsatsa

Nde mukapeza ka ndalama Sister, chonde kumakagwiritsitsa
Mukamagona nako kukafunditsa
Kwachuluka mbava nde muzikabisa
Yi, ndikupempha mundithandize

Yi, wangondivuta ndi uphawi [Ayi
Ah, ah
Akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
Akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje

Ulendo wanga ukathera ku Lilongwe, m’deport
Koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje
Inu ulendo wanga ukathera ku Lilongwe, m’deport
Koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje, yi

Aish, conductor pokwera umati 100 ndangokhala pansi ukuti 120
Aseh, osaziyamba zin#z#
Muno sindichoka ngati sundipatsa change
Wekha ukudziwa dollar ili pa minga

Povaya kudedza pena kukwera njinga
Umayesa ngati ukundiyimba
Lero lonkha wandilira sindiyimva
Yi, ndikupempha mundithandize

Yi, wangondivuta ndi uphawi [Ayi
Ah, ah
Akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
Akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje

Ulendo wanga ukathera ku Lilongwe, m’deport
Koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje
Inu ulendo wanga ukathera ku Lilongwe, m’deport
Koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje, yi

Aish, komanso Yesu akufuna change mama
Koma change akufuna iye si ndalama
Akufunitsitsa inuyo makamaka mutasintha ndikuyamba kumutsata
Mapemphero ndi hustle ya uzimu

Mukapusa tsiku lomaliza, no change
Mapemphero ndi hustle ya uzimu
Ukapusa tsiku lomaliza, no change
Yi, ndikupempha mundithandize

Yi, wangondivuta ndi umphawi
Ah, ah
Akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje
Akondakitale ndalama ndalipilayi ndati ndipemphe, mundibwenzereko chenje

Ulendo wanga ukathera ku Lilongwe, m’deport
Koma ndipemphe, mundibwenzereko change
Inu ulendo wanga ukathera ku Lilongwe, m’deport
Koma ndipemphe, mundibwenzereko chenje, yi
Find more lyrics at lyrics.jspinyin.net

You can purchase their music thru 
Amazon Music or Apple Music
Disclosure: As an Amazon Associate and an Apple Partner, we earn from qualifying purchases
Other Popular Songs:
Hillsong - Sing of Your Great Love
Azahriah - Disday

Akondakitale – English Translation

Yi, Aye-he-yah
Aye-he-yah
Favoritsomers Followersi Followed I will ask, please enter the witness
Favoritsomers Followersi Followed I will ask, please enter the witness

When my trip has ended in Lilongwe, drive
But I will ask you, please come you out of it
When you make my journey to Lilongwe, drive
But I will ask you, please, too, as a witness, yi

Aish, the money in the arms
Daily Fans to search
Don’t see that you’re shasha
Business Business only is advertising

When you get a safer investment, please hold on to
When you lie in the narrower
Has increased and be scattered
Yi, i request help me

Yi, you just struggle with my reusives
Ah, ah
Favoritsomers Followersi Followed I will ask, please enter the witness
Favoritsomers Followersi Followed I will ask, please enter the witness

When my trip has ended in Lilongwe, drive
But I will ask you, please come you out of it
When you make my journey to Lilongwe, drive
But I will ask you, please, too, as a witness, yi

Aish, CDUCOCOKY PLANTED 100 IT HAPPEN DIFFERED AT BIGHT BOSE ARE YOU
ASEH, don’t starve
In the morning I don’t get off if you don’t give me a Change
Only know dollar is on thorns

Povaya to come on a bicycle
You try if you’re going to call me
Today’s tapped me don’t feel
Yi, i request help me

Yi, you just struggle with my reusives
Ah, ah
Favoritsomers Followersi Followed I will ask, please enter the witness
Favoritsomers Followersi Followed I will ask, please enter the witness

When my trip has ended in Lilongwe, drive
But I will ask you, please come you out of it
When you make my journey to Lilongwe, drive
But I will ask you, please, too, as a witness, yi

Aish, as well as Jesus wishes for mama
But Change wants her not money
Is eager to you especially after you change and start following you
Prayers and Hustle Hustle

When you are f#cking the last day, no Change
Prayers and Hustle Hustle
If you are foolish in the last day, no Change
Yi, i request help me

Yi, you just challenged me with poverty
Ah, ah
Favoritsomers Followersi Followed I will ask, please enter the witness
Favoritsomers Followersi Followed I will ask, please enter the witness

When my trip has ended in Lilongwe, drive
But I’ll ask you, get you back in Change
When you make my journey to Lilongwe, drive
But I will ask you, please, too, as a witness, yi
Find more lyrics at lyrics.jspinyin.net

Lyrics Gwamba – Akondakitale

Kindly like and share our content. Please follow our site to get the latest lyrics for all songs.

We don’t provide any MP3 Download, please support the artist by purchasing their music 🙂

You can purchase their music thru 
Amazon Music or Apple Music
Disclosure: As an Amazon Associate and an Apple Partner, we earn from qualifying purchases

https://www.youtube.com/watch?v=HamSrjn2VPE